Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Mateyu 27:33 - Buku Lopatulika

33 Ndipo pamene anadza kumalo dzina lake Gologota, ndiko kunena kuti, Malo a Bade,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

33 Ndipo pamene anadza kumalo dzina lake Gologota, ndiko kunena kuti, Malo a Bade,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

33 Ndipo adafika ku malo otchedwa Gologota, (ndiye kuti “Malo a Chibade cha Mutu.”)

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

33 Anafika ku malo wotchedwa Gologota amene atanthauza kuti malo a bade la mutu.

Onani mutuwo Koperani




Mateyu 27:33
6 Mawu Ofanana  

Ndipo pa ora lachisanu ndi chinai Yesu anafuula ndi mau okweza, Eloi, Eloi, lama sabakitani? ndiko kusandulika, Mulungu wanga, Mulungu wanga mwandisiyiranji Ine?


Ndipo ora lake pamenepo linali ngati lachisanu ndi chimodzi. Ndipo panali mdima padziko lonse kufikira ora lachisanu ndi chinai, ndipo dzuwa linada.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa