Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Mateyu 27:28 - Buku Lopatulika

28 Ndipo anavula malaya ake, namveka malaya ofiira achifumu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

28 Ndipo anavula malaya ake, namveka malaya ofiira achifumu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

28 Adamuvula zovala zake, namuveka chovala chofiira.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

28 Anamuvula malaya ake namuveka Iye malaya ofiira aufumu.

Onani mutuwo Koperani




Mateyu 27:28
4 Mawu Ofanana  

Ndipo anamveka Iye chibakuwa, naluka korona waminga, namveka pa Iye;


Ndipo Herode ndi asilikali ake anampeputsa Iye, namnyoza, namveka Iye chofunda chonyezimira, nambwezera kwa Pilato.


Ndipo ananditenga kunka nane kuchipululu, mu Mzimu; ndipo ndinaona mkazi alinkukhala pachilombo chofiira, chodzala ndi maina a mwano, chakukhala nayo mitu isanu ndi iwiri ndi nyanga khumi.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa