Mateyu 26:67 - Buku Lopatulika67 Pomwepo iwo anathira malovu pankhope pake, nambwanyula Iye; ndipo ena anampanda khofu, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201467 Pomwepo iwo anathira malovu pankhope pake, nambwanyula Iye; ndipo ena anampanda khofu, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa67 Pomwepo iwo adayamba kumthira malovu kumaso nkumamumenya, ena kumamuwomba makofi, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero67 Kenaka anamulavulira kumaso namumenya ndi zibakera. Ena anamumenya makofi. Onani mutuwo |