Mateyu 25:43 - Buku Lopatulika43 ndinali mlendo, ndipo simunandilandire Ine; wamaliseche ndipo simunandiveke Ine; wodwala, ndi m'nyumba yandende, ndipo simunadze kundiona Ine. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201443 ndinali mlendo, ndipo simunandilandira Ine; wamaliseche ndipo simunandiveka Ine; wodwala, ndi m'nyumba yandende, ndipo simunadza kundiona Ine. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa43 Ndidaali mlendo, inu osandilandira kunyumba kwanu. Ndidaali wamaliseche, inu osandiveka. Ndinkadwala, ndidaalinso m'ndende, inu osadzandichetsa.’ Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero43 ndinali mlendo koma inu simunandilandire, ndinali wa usiwa koma simunandiveke, ndinali wodwala komanso ku ndende simunandisamalire.’ Onani mutuwo |