Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Mateyu 25:19 - Buku Lopatulika

19 Ndipo itapita nthawi yaikulu, anabwera mbuye wa akapolo awo, nawerengera nao pamodzi.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

19 Ndipo itapita nthawi yaikulu, anabwera mbuye wa akapolo awo, nawerengera nao pamodzi.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

19 “Patapita nthaŵi yaitali, mbuye wao uja adabwerako naŵaitana antchito ake aja kuti amufotokozere za zimene adaachita ndi ndalama zija.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

19 “Patapita nthawi yayitali, mbuye wa antchitowo anabwera nawayitana kuti afotokoze chimene anachita ndi ndalama zija.

Onani mutuwo Koperani




Mateyu 25:19
11 Mawu Ofanana  

Koma kapolo woipa akanena mumtima mwake, Mbuye wanga wachedwa;


Koma uyo amene analandira imodziyo anamuka, nakumba pansi, naibisa talente ya mbuye wake.


Ndipo pamene mkwati anachedwa, onsewo anaodzera, nagona tulo.


Monganso Davide anena za mdalitso wake wa munthu, amene Mulungu amwerengera chilungamo chopanda ntchito,


Pakuti ife tonse tiyenera kuonetsedwa kumpando wakuweruza wa Khristu, kuti yense alandire zochitika m'thupi, monga momwe anachita, kapena chabwino kapena choipa.


Musakhale aphunzitsi ambiri, abale anga, podziwa kuti tidzalangika koposa.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa