Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Mateyu 25:18 - Buku Lopatulika

18 Koma uyo amene analandira imodziyo anamuka, nakumba pansi, naibisa talente ya mbuye wake.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

18 Koma uyo amene analandira imodziyo anamuka, nakumba pansi, naibisa talente ya mbuye wake.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

18 Koma amene adaalandira ndalama imodzi uja, adapita nakaikumbira pansi ndalama ya mbuye wake ija.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

18 Koma munthu amene analandira 1,000 uja, anapita nakumba dzenje nabisapo ndalama ya mbuye wake.

Onani mutuwo Koperani




Mateyu 25:18
9 Mawu Ofanana  

Wogwira ntchito mwaulesi ndiye mbale wake wa wosakaza.


Mwenzi atakhala wina mwa inu wakutseka pamakomo, kuti musasonkhe moto chabe paguwa langa la nsembe! Sindikondwera nanu, ati Yehova wa makamu, ndipo sindidzalandira chopereka m'dzanja lanu.


Chimodzimodzi uyo wa awiriwo, anapindulapo ena awiri.


Ndipo itapita nthawi yaikulu, anabwera mbuye wa akapolo awo, nawerengera nao pamodzi.


Ndipo wina anadza, nanena, Mbuye, taonani, siyi mina yanu, ndaisunga m'kansalu;


kuti musakhale aulesi, koma akuwatsanza iwo amene alikulowa malonjezano mwa chikhulupiriro ndi kuleza mtima.


Pakuti izi zikakhala ndi inu, ndipo zikachuluka, zidzachita kuti musakhale aulesi kapena opanda zipatso pa chizindikiritso cha Ambuye Yesu Khristu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa