Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Mateyu 25:17 - Buku Lopatulika

17 Chimodzimodzi uyo wa awiriwo, anapindulapo ena awiri.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

17 Chimodzimodzi uyo wa awiriwo, anapindulapo ena awiri.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

17 Chimodzimodzinso amene adaalandira ndalama ziŵiri uja, adapindula ndalama zinanso ziŵiri.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

17 Chimodzimodzinso amene analandira 2,000 uja anapindula 2,000 zina.

Onani mutuwo Koperani




Mateyu 25:17
23 Mawu Ofanana  

Chifukwa ndamdziwa iye kuti alamulire ana ake ndi banja lake la pambuyo pake, kuti asunge njira ya Yehova, kuchita chilungamo ndi chiweruziro, kuti Yehova akamtengere Abrahamu chomwe anamnenera iye.


Ndipo Barizilai anali nkhalamba, ndiye wa zaka makumi asanu ndi atatu; ndiye amene anapereka chakudya kwa mfumu muja anagona ku Mahanaimu, pakuti anali munthu womveka ndithu.


Pomwepo uyo amene analandira matalente asanu, anapita kugula nazo malonda, napindulapo matalente ena asanu.


Koma uyo amene analandira imodziyo anamuka, nakumba pansi, naibisa talente ya mbuye wake.


ndiye munthu wopembedza, ndi wakuopa Mulungu ndi banja lake lonse, amene anapatsa anthu zachifundo zambiri, napemphera Mulungu kosaleka.


Pakuti ngati chivomerezocho chili pomwepo, munthu alandiridwa monga momwe ali nacho, si monga chimsowa.


akuchita machawi, popeza masiku ali oipa.


Ndipo nenani kwa Arkipo, Samaliratu utumiki umene udaulandira mwa Ambuye, kuti uukwanitse.


wa mbiri ya ntchito zabwino; ngati walera ana, ngati wachereza alendo, ngati adasambitsa mapazi a oyera mtima, ngati wathandiza osautsidwa, ngati anatsatadi ntchito zonse zabwino.


monga yense walandira mphatso, mutumikirane nayo, ngati adindo okoma a chisomo cha mitundumitundu cha Mulungu;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa