Mateyu 25:17 - Buku Lopatulika17 Chimodzimodzi uyo wa awiriwo, anapindulapo ena awiri. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201417 Chimodzimodzi uyo wa awiriwo, anapindulapo ena awiri. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa17 Chimodzimodzinso amene adaalandira ndalama ziŵiri uja, adapindula ndalama zinanso ziŵiri. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero17 Chimodzimodzinso amene analandira 2,000 uja anapindula 2,000 zina. Onani mutuwo |