Mateyu 25:14 - Buku Lopatulika14 Pakuti monga munthu, wakunka ulendo, aitana akapolo ake, napereka kwa iwo chuma chake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Pakuti monga munthu, wakunka ulendo, aitana akapolo ake, napereka kwa iwo chuma chake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 “Za Ufumu wakumwamba tingazifanizirenso motere: Munthu wina ankapita pa ulendo. Asananyamuke adaitana antchito ake, naŵasiyira chuma chake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 “Komanso udzafanizidwa ndi munthu amene ankapita pa ulendo, ndipo anayitana antchito ake nawasiyira chuma chake. Onani mutuwo |