Mateyu 24:37 - Buku Lopatulika37 Ndipo monga masiku a Nowa, kotero kudzakhala kufika kwake kwa Mwana wa Munthu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201437 Ndipo monga masiku a Nowa, kotero kudzakhala kufika kwake kwa Mwana wa Munthu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa37 Kudza kwa Mwana wa Munthu kudzakhala monga momwe zinthu zidaayendera pa nthaŵi ya Nowa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero37 Monga momwe zinalili nthawi ya Nowa, momwemonso zidzatero pobwera kwa Mwana wa Munthu. Onani mutuwo |