Mateyu 23:38 - Buku Lopatulika38 Onani, nyumba yanu yasiyidwa kwa inu yabwinja. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201438 Onani, nyumba yanu yasiyidwa kwa inu yabwinja. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa38 Ndithu nyumba yanu yaikuluyi idzasanduka bwinja. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero38 Taona, nyumba yako yasiyidwa ya bwinja. Onani mutuwo |
Ndipo atapita masabata makumi asanu ndi limodzi mphambu awiri wodzozedwayo adzalikhidwa, nadzakhala wopanda kanthu; ndi anthu a kalonga wakudzayo adzaononga mzinda ndi malo opatulika; ndi kutsiriza kwake kudzakhala kwa chigumula, ndi kufikira chimaliziro kudzakhala nkhondo; chipasuko chalembedweratu.