Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Mateyu 23:36 - Buku Lopatulika

36 Indetu ndinena kwa inu, Zinthu zonse izi zidzafika pa mbadwo uwu wamakono.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

36 Indetu ndinena kwa inu, Zinthu zonse izi zidzafika pa mbadwo uwu wamakono.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

36 Ndithu ndikunenetsa kuti chilango cha zonsezi chidzaŵagwera ndithu anthu amakonoŵa.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

36 Zoonadi, ndikuwuzani kuti zonsezi zidzafika pa mʼbado uno.

Onani mutuwo Koperani




Mateyu 23:36
5 Mawu Ofanana  

Koma pamene angakuzunzeni inu m'mudzi uwu, thawirani mwina: indetu ndinena kwa inu, Simudzaitha mizinda ya Israele, kufikira Mwana wa Munthu atadza.


Indetu ndinena kwa inu, mbadwo uwu sudzatha kuchoka, kufikira zinthu zonsezi zidzachitidwa.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa