Mateyu 23:28 - Buku Lopatulika28 Chomwecho inunso muonekera olungama pamaso pa anthu, koma m'kati muli odzala ndi chinyengo ndi kusaweruzika. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201428 Chomwecho inunso muonekera olungama pamaso pa anthu, koma m'kati muli odzala ndi chinyengo ndi kusaweruzika. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa28 Inunso muli chimodzimodzi: pamaso pa anthu mumaoneka olungama, pamene m'kati mwanu m'modzaza ndi chiphamaso ndi zoipa zina. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero28 Chimodzimodzinso, kunja mumaoneka kwa anthu kuti ndinu olungama koma mʼkatimo ndinu odzaza ndi chinyengo ndi zoyipa zina. Onani mutuwo |