Mateyu 21:45 - Buku Lopatulika45 Ndipo ansembe aakulu ndi Afarisi, pakumva mafanizo ake, anazindikira kuti alikunena za iwo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201445 Ndipo ansembe aakulu ndi Afarisi, pakumva mafanizo ake, anazindikira kuti alikunena za iwo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa45 Pamene akulu a ansembe ndi Afarisi adamva mafanizo ameneŵa a Yesu, adazindikira kuti ankanena iwowo, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero45 Akulu a ansembe ndi Afarisi atamva mafanizo a Yesu, anadziwa kuti ankanena iwo. Onani mutuwo |