Mateyu 21:37 - Buku Lopatulika37 Koma pambuyo pake anatumiza kwa iwo mwana wake, nati, Adzachitira mwana wanga ulemu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201437 Koma pambuyo pake anatumiza kwa iwo mwana wake, nati, Adzachitira mwana wanga ulemu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa37 Potsiriza pake adaŵatumira mwana wake, nanena kuti, ‘Mwana wanga yekhayu akamchitira ulemu.’ Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero37 Pomalizira anatumiza mwana wake. Anati adzamuchitira ulemu mwana wanga. Onani mutuwo |