Mateyu 21:15 - Buku Lopatulika15 Koma ansembe aakulu ndi alembi, m'mene anaona zozizwitsa zomwe Iye anazichita, ndi ana alinkufuula ku Kachisiko kuti, Hosana kwa Mwana wa Davide, anapsa mtima, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201415 Koma ansembe aakulu ndi alembi, m'mene anaona zozizwitsa zomwe Iye anazichita, ndi ana alinkufuula ku Kachisiko kuti, Hosana kwa Mwana wa Davide, anapsa mtima, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa15 Akulu a ansembe ndi aphunzitsi a Malamulo adaona zodabwitsa zimene Iye ankachita. Adamvanso ana akufuula m'Nyumba ya Mulungu kuti, “Ulemu kwa Mwana wa Davide.” Ndiye iwowo adapsa nazo mtima, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero15 Koma akulu a ansembe ndi aphunzitsi amalamulo ataona zodabwitsa zimene anachita, komanso ana akufuwula mʼNyumbayo kuti, “Hosana kwa Mwana wa Davide,” anapsa mtima. Onani mutuwo |