Mateyu 19:20 - Buku Lopatulika20 Mnyamatayo ananena kwa Iye, Zonsezi ndinazisunga, ndisowanso chiyani? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201420 Mnyamatayo ananena kwa Iye, Zonsezi ndinazisunga, ndisowanso chiyani? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa20 Munthu uja adati, “Malamulo onseŵa ndakhala ndikuŵatsata, nanga chanditsaliranso nchiyani?” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero20 Mnyamatayo anati, “Zonsezi ndimazisunga, nanga chatsala ndi chiyani?” Onani mutuwo |