Mateyu 16:28 - Buku Lopatulika28 Indetu ndinena kwa inu, kuti alipo ena a iwo aima pano sadzalawa ndithu imfa, kufikira adzaona Mwana wa Munthu atadza mu ufumu wake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201428 Indetu ndinena kwa inu, kuti alipo ena a iwo aima pano sadzalawa ndithu imfa, kufikira adzaona Mwana wa Munthu atadza mu ufumu wake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa28 Ndithu ndikunenetsa kuti alipo ena pompano omwe sadzafa asanaone Mwana wa Munthu akubwera ndi ulemerero waufumu.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero28 “Ine ndikuwuzani inu choonadi, ena amene akuyimirira pano sadzalawa imfa asanaone Mwana wa Munthu akudza mu ufumu.” Onani mutuwo |