Mateyu 15:37 - Buku Lopatulika37 Ndipo onsewa anadya, nakhuta: ndipo anatola makombo otsala madengu asanu ndi awiri odzala. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201437 Ndipo onsewa anadya, nakhuta: ndipo anatola makombo otsala madengu asanu ndi awiri odzala. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa37 Anthu onsewo adadya mpaka kukhuta. Adatola zotsala, nkudzaza madengu asanu ndi aŵiri. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero37 Onse anadya ndipo anakhuta. Pomaliza ophunzira anatolera zotsalira nadzaza madengu asanu ndi awiri. Onani mutuwo |