Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Mateyu 14:35 - Buku Lopatulika

35 Ndipo m'mene amuna a pamenepo anamzindikira, anatumiza konse kudziko lonse lozungulira, nadza nao kwa Iye onse akukhala ndi nthenda;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

35 Ndipo m'mene amuna a pamenepo anamzindikira, anatumiza konse kudziko lonse lozungulira, nadza nao kwa Iye onse akukhala ndi nthenda;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

35 Anthu akumeneko adamzindikira Yesu, nakadziŵitsa anzao a ku dera lonse lozungulira pamenepo. Motero adadza kwa Yesu ndi anthu onse odwala.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

35 Anthu akumeneko atamuzindikira Yesu, iwo anatumiza mawu kwa onse ozungulira deralo. Anthu anabwera ndi odwala awo onse kwa Iye.

Onani mutuwo Koperani




Mateyu 14:35
9 Mawu Ofanana  

Ndipo pamene iwo anaoloka, anafika kumtunda, ku Genesarete.


ndipo anampempha Iye, kuti akhudze mphonje yokha ya chovala chake; ndipo onse amene anamkhudza anachiritsidwa.


nathamangira dziko lonselo nayamba kunyamula anthu odwala pa mphasa zao, kufika nao kumene anamva kuti analiko Iye.


Ndipo pozindikira mau ake a Petro, chifukwa cha kukondwera sanatsegule pakhomo, koma anathamanga nalowanso, nawauza kuti Petro alikuima pakhomo.


namzindikira iye, kuti ndiye amene anakhala pa Chipata Chokongola cha Kachisi: ndipo anadzazidwa ndi kudabwa ndi kuzizwa pa ichi chidamgwera.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa