Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Mateyu 13:58 - Buku Lopatulika

58 Ndipo Iye, chifukwa cha kusakhulupirira kwao, sanachite kumeneko zamphamvu zambiri.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

58 Ndipo Iye, chifukwa cha kusakhulupirira kwao, sanachite kumeneko zamphamvu zambiri.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

58 Motero sadachite zamphamvu zambiri kumeneko, chifukwa cha kusakhulupirira kwa anthuwo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

58 Ndipo Iye sanachite zodabwitsa zambiri kumeneko chifukwa cha kusowa kwa chikhulupiriro kwawo.

Onani mutuwo Koperani




Mateyu 13:58
7 Mawu Ofanana  

Ndipo iwo anakhumudwa chifukwa cha Iye. Koma Yesu anati kwa iwo, Mneneri sakhala wopanda ulemu koma kudziko la kwao ndiko, ndi kubanja kwake.


Nthawi imeneyo Herode mfumu anamva mbiri ya Yesu,


Chabwino; iwo anathyoledwa ndi kusakhulupirira kwao, ndipo iwe umaima ndi chikhulupiriro chako. Usamadzikuza mumtima, koma opatu:


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa