Mateyu 12:50 - Buku Lopatulika50 Pakuti aliyense amene adzachita chifuniro cha Atate wanga wa Kumwamba, yemweyo ndiye mbale wanga, ndi mlongo wanga, ndi amai wanga. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201450 Pakuti aliyense amene adzachita chifuniro cha Atate wanga wa Kumwamba, yemweyo ndiye mbale wanga, ndi mlongo wanga, ndi amai wanga. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa50 Pakuti aliyense wochita zimene Atate anga akumwamba akufuna, ameneyo ndiye mbale wanga ndi mlongo wanga ndi amai anga.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero50 Pakuti aliyense amene achita chifuniro cha Atate anga akumwamba ndiye mʼbale wanga, mlongo wanga ndi amayi anga.” Onani mutuwo |