Mateyu 12:43 - Buku Lopatulika43 Koma mzimu wonyansa, utatuluka mwa munthu, umapitirira malo opanda madzi kufunafuna mpumulo, osaupeza. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201443 Koma mzimu wonyansa, utatuluka mwa munthu, umapitirira malo opanda madzi kufunafuna mpumulo, osaupeza. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa43 “Mzimu woipa ukatuluka mwa munthu, umakayendayenda ku malo opanda madzi, kufunafuna malo opumulirako, koma osaŵapeza. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero43 “Pamene mzimu woyipa utuluka mwa munthu, umadutsa malo wopanda madzi kufunafuna malo opumulira ndipo suwapeza. Onani mutuwo |