Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Mateyu 12:37 - Buku Lopatulika

37 Pakuti udzayesedwa wolungama ndi mau ako, ndipo ndi mau ako omwe udzatsutsidwa.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

37 Pakuti udzayesedwa wolungama ndi mau ako, ndipo ndi mau ako omwe udzatsutsidwa.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

37 Mwakuti chifukwa cha mau ako omwe mlandu udzakukomera kapena kukuipira.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

37 Pakuti ndi mawu anu mudzapezeka osalakwa ndiponso ndi mawu anu mudzapezeka olakwa.”

Onani mutuwo Koperani




Mateyu 12:37
5 Mawu Ofanana  

Wogwira pakamwa pake asunga moyo wake; koma woyasamula milomo yake adzaonongeka.


Lilime lili ndi mphamvu pa imfa ndi moyo; wolikonda adzadya zipatso zake.


Ndipo ndinena kwa inu, kuti mau onse opanda pake, amene anthu adzalankhula, adzawawerengera mlandu wake tsiku la kuweruza.


Pomwepo alembi ndi Afarisi ena anayankha Iye nati, Mphunzitsi, tifuna kuona chizindikiro cha Inu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa