Mateyu 12:35 - Buku Lopatulika35 Munthu wabwino atulutsa zabwino m'chuma chake chabwino, ndi munthu woipa atulutsa zoipa m'chuma chake choipa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201435 Munthu wabwino atulutsa zabwino m'chuma chake chabwino, ndi munthu woipa atulutsa zoipa m'chuma chake choipa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa35 Munthu wabwino amatulutsa zabwino m'chuma chabwino cha mumtima mwake. Nayenso munthu woipa amatulutsa zoipa m'chuma choipa cha mumtima mwake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero35 Munthu wabwino amatulutsa zinthu zabwino zomwe zili mumtima mwake ndipo munthu woyipa amatulutsanso zinthu zoyipa zomwe zili mwa iye. Onani mutuwo |