Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Masalimo 98:7 - Buku Lopatulika

7 Nyanja ifuule ndi kudzala kwake; dziko lokhalamo anthu ndi iwo okhalamo;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

7 Nyanja ifuule ndi kudzala kwake; dziko lokhalamo anthu ndi iwo okhalamo;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

7 Nyanja ikokome pamodzi ndi zonse zam'menemo, dziko lifuule pamodzi ndi anthu onse am'menemo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

7 Nyanja ikokome pamodzi ndi zonse zili mʼmenemo, dziko lonse ndi onse amene amakhala mʼmenemo.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 98:7
4 Mawu Ofanana  

Dziko lapansi nla Yehova ndi zodzala zake zomwe, dziko lokhalamo anthu ndi iwo okhala m'mwemo.


Kumwamba kukondwere nilisekerere dziko lapansi; nyanja ibume mwa kudzala kwake.


Imbani inu, m'mwamba, nukondwere iwe dziko lapansi, imbani inu mapiri, pakuti Yehova watonthoza mtima wa anthu ake, nadzachitira chifundo ovutidwa ake.


Pakuti monga dziko liphukitsa mphundu zake, ndi monga munda umeretsa zobzalamo, momwemo Ambuye Yehova adzaphukitsa chilungamo ndi matamando pamaso pa amitundu onse.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa