Masalimo 98:6 - Buku Lopatulika6 Fuulani pamaso pa Mfumu Yehova, ndi mbetete ndi liu la lipenga. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Fuulani pamaso pa Mfumu Yehova, ndi mbetete ndi liu la lipenga. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Imbirani Chauta Mfumu, imbani molimbika ndi malipenga ndi mbetete. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 ndi malipenga ndi kuliza kwa nyanga ya nkhosa yayimuna fuwulani mwachimwemwe pamaso pa Yehova Mfumu. Onani mutuwo |