Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Masalimo 98:5 - Buku Lopatulika

5 Muimbireni Yehova zomlemekeza ndi zeze; ndi zeze ndi mau a salimo.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

5 Muimbireni Yehova zomlemekeza ndi zeze; ndi zeze ndi mau a salimo.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

5 Imbani nyimbo zoyamika Chauta ndi pangwe, lizani pangwe ndi nyimbo zokoma.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

5 Imbirani Yehova nyimbo ndi zeze, ndi zeze ndi mawu a kuyimba,

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 98:5
11 Mawu Ofanana  

Ndipo Davide ananena ndi mkulu wa Alevi kuti aike abale ao oimbawo ndi zoimbira, zisakasa, ndi azeze, ndi nsanje, azimveketse ndi kukweza mau ao ndi chimwemwe.


Momwemo Aisraele onse anakwera nalo likasa la chipangano la Yehova ndi kufuula, ndi kumveka kwa lipenga, ndi mphalasa, ndi nsanje zomveketsa, ndi zisakasa, ndi azeze.


Ndipo anaika Alevi m'nyumba ya Yehova ndi nsanje, ndi zisakasa, ndi azeze, monga umo adauzira Davide, ndi Gadi mlauli wa mfumu, ndi Natani mneneriyo; pakuti lamulo ili lidafuma kwa Yehova mwa aneneri ake.


Yamikani Yehova ndi kuthira mang'ombe; muimbireni Mulungu wathu zomlemekeza pazeze:


Yamikani Yehova ndi zeze; muimbireni ndi chisakasa cha zingwe khumi.


Ndiponso ndidzakuyamikani ndi chisakasa, kubukitsa choonadi chanu, Mulungu wanga; ndidzakuimbirani nyimbo ndi zeze, ndinu Woyerayo wa Israele.


Pakuti Yehova watonthoza mtima wa Ziyoni, watonthoza mtima wa malo ake onse abwinja; ndipo wasandutsa chipululu chake ngati Edeni, ndi malo ake ouma ngati munda wa Yehova; kukondwa ndi kusangalala kudzapezedwa m'menemo, mayamikiro, ndi mau a nyimbo yokoma.


Ndipo pamene adatenga bukulo, zamoyo zinai ndi akulu makumi awiri mphambu anai zinagwa pansi pamaso pa Mwanawankhosa, zonse zili nao azeze, ndi mbale zagolide zodzala ndi zofukiza, ndizo mapemphero a oyera mtima.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa