Masalimo 98:5 - Buku Lopatulika5 Muimbireni Yehova zomlemekeza ndi zeze; ndi zeze ndi mau a salimo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Muimbireni Yehova zomlemekeza ndi zeze; ndi zeze ndi mau a salimo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Imbani nyimbo zoyamika Chauta ndi pangwe, lizani pangwe ndi nyimbo zokoma. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Imbirani Yehova nyimbo ndi zeze, ndi zeze ndi mawu a kuyimba, Onani mutuwo |