Masalimo 95:8 - Buku Lopatulika8 Musaumitse mitima yanu, ngati ku Meriba, ngati tsiku la ku Masa m'chipululu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Musaumitse mitima yanu, ngati ku Meriba, ngati tsiku la ku Masa m'chipululu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Musaumitse mitima yanu monga ku Meriba kuja, monganso tsiku lija ku Masa m'chipululu muja, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 musawumitse mitima yanu monga momwe munachitira pa Meriba, monga munachitira tsiku lija pa Masa mʼchipululu. Onani mutuwo |