Masalimo 95:4 - Buku Lopatulika4 Malo ozama a dziko lapansi ali m'dzanja lake; chuma cha m'mapiri chomwe ndi chake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Malo ozama a dziko lapansi ali m'dzanja lake; chuma cha m'mapiri chomwe ndi chake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Maziko ozama a dziko lapansi ali m'manja mwake. Mapiri aatali omwe ngakenso. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Mʼmanja mwake muli maziko ozama a dziko lapansi, ndipo msonga za mapiri ndi zake. Onani mutuwo |