Masalimo 94:21 - Buku Lopatulika21 Asonkhana pamodzi pa moyo wa wolungama, namtsutsa wa mwazi wosachimwa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201421 Asonkhana pamodzi pa moyo wa wolungama, namtsutsa wa mwazi wosachimwa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa21 Amagwirizana kuti aononge anthu osalakwa, nagamula kuti opanda mlandu aphedwe. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero21 Iwo amasonkhana pamodzi kulimbana ndi wolungama ndi kugamula kuti wosalakwa aphedwe. Onani mutuwo |