Masalimo 94:20 - Buku Lopatulika20 Kodi uyenera kuyanjana ndi Inu mpando wachifumu wa kusakaza, wakupanga chovuta chikhale lamulo? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201420 Kodi uyenera kuyanjana ndi Inu mpando wachifumu wa kusakaza, wakupanga chovuta chikhale lamulo? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa20 Kodi angathe kugwirizana nanu olamulira oipa, amene amapotoza malamulo anu olungama? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero20 Kodi mpando waufumu woyipa ungathe kugwirizana nanu umene umabweretsa masautso chifukwa cha malamulo ake? Onani mutuwo |