Masalimo 94:19 - Buku Lopatulika19 Pondichulukira zolingalira zanga m'kati mwanga, zotonthoza zanu zikondweretsa moyo wanga. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201419 Pondichulukira zolingalira zanga m'kati mwanga, zotonthoza zanu zikondweretsa moyo wanga. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa19 Pamene nkhaŵa zikundichulukira, Inu mumasangalatsa mtima wanga. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero19 Pamene nkhawa inakula mʼkati mwanga, chitonthozo chanu chinabweretsa chimwemwe mʼmoyo mwanga. Onani mutuwo |