Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Masalimo 94:18 - Buku Lopatulika

18 Pamene ndinati, Literereka phazi langa, chifundo chanu, Yehova, chinandichirikiza.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

18 Pamene ndinati, Litereka phazi langa, chifundo chanu, Yehova, chinandichirikiza.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

18 Pamene ndinkaganiza kuti, “Phazi langa likuterereka,” nkuti chikondi chanu chosasinthika chikundichirikiza.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

18 Ndikanena kuti, “Phazi langa likuterereka,” chikondi chanu, Inu Yehova, chimandichirikiza.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 94:18
11 Mawu Ofanana  

Sadzalola phazi lako literereke: Iye amene akusunga sadzaodzera.


M'mayendedwe anga ndasunga mabande anu, mapazi anga sanaterereke.


Pakuti ndinati, Asakondwerere ine; pakuterereka phazi langa, asadzikuze pa ine.


Koma ine, ndikadagwa; mapazi anga akadaterereka.


usaope, pakuti Ine ndili pamodzi ndi iwe; usaopsedwe, pakuti Ine ndine Mulungu wako; ndidzakulimbitsa; inde, ndidzakuthangata; inde, ndidzakuchirikiza ndi dzanja langa lamanja la chilungamo.


koma ndinakupempherera kuti chikhulupiriro chako chingazime; ndipo iwe, pamene watembenuka ukhazikitse abale ako.


Nanga mafuta onunkhira awa sanagulitsidwe chifukwa ninji ndi marupiya atheka mazana atatu, ndi kupatsidwa kwa osauka?


amene musungidwa ndi mphamvu ya Mulungu mwa chikhulupiriro, kufikira chipulumutso chokonzeka kukavumbulutsidwa nthawi yotsiriza.


Adzasunga mapazi a okondedwa ake, koma oipawo adzawakhalitsa chete mumdima; pakuti palibe munthu adzapambana ndi mphamvu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa