Masalimo 94:14 - Buku Lopatulika14 Pakuti Yehova sadzasiya anthu ake, ndipo sadzataya cholowa chake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Pakuti Yehova sadzasiya anthu ake, ndipo sadzataya cholandira chake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Chauta sadzaŵataya anthu ake, sadzaŵasiya okha osankhidwa ake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 Pakuti Yehova sadzawakana anthu ake; Iye sadzasiya cholowa chake. Onani mutuwo |