Masalimo 94:13 - Buku Lopatulika13 kuti mumpumitse masiku oipa; kufikira atakumbira woipa mbuna. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 kuti mumpumitse masiku oipa; kufikira atakumbira woipa mbuna. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Mumampumitsa pa nthaŵi yamavuto, mpaka woipa ataloŵa m'dzenje. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 mumamupumitsa pa nthawi ya mavuto, mpaka woyipa atakumbiridwa dzenje. Onani mutuwo |