Masalimo 91:6 - Buku Lopatulika6 kapena mliri woyenda mumdima, kapena chionongeko chakuthera usana. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 kapena mliri woyenda mumdima, kapena chionongeko chakuthera usana. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Sudzaopanso mliri wogwa usiku, kapena zoononga moyo masana. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 kapena mliri umene umayenda mu mdima, kapena zowononga za pa nthawi ya masana. Onani mutuwo |