Masalimo 91:13 - Buku Lopatulika13 Udzaponda mkango ndi mphiri; udzapondereza msona wa mkango ndi chinjoka. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Udzaponda mkango ndi mphiri; udzapondereza msona wa mkango ndi chinjoka. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Udzatha kuponda mkango ndi njoka, zoonadi udzaponda ndi phazi lako msona wa mkango ndiponso chinjoka. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Udzapondaponda mkango ndi njoka, udzapondereza mkango wamphamvu ndiponso chinjoka. Onani mutuwo |