Masalimo 90:16 - Buku Lopatulika16 Chochita Inu chioneke kwa atumiki anu, ndi ulemerero wanu pa ana ao. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 Chochita Inu chioneke kwa atumiki anu, ndi ulemerero wanu pa ana ao. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 Mulole kuti ntchito zanu ziwoneke kwa atumiki anu, mphamvu zanu zaulemerero ziwoneke kwa ana ao. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 Ntchito zanu zionetsedwe kwa atumiki anu, kukongola kwanu kwa ana awo. Onani mutuwo |