Masalimo 90:14 - Buku Lopatulika14 Mutikhutitse nacho chifundo chanu m'mawa; ndipo tidzafuula mokondwera ndi kukondwera masiku athu onse. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Mutikhutitse nacho chifundo chanu m'mawa; ndipo tidzafuula mokondwera ndi kukondwera masiku athu onse. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Tidzazeni m'maŵa mulimonse ndi chikondi chanu chosasinthika, kuti tizikondwa ndi kusangalala masiku athu onse. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 Mutikhutitse mmawa ndi chikondi chanu chosatha, kuti tiyimbe ndi chimwemwe ndi kukhala okondwa masiku athu onse. Onani mutuwo |