Masalimo 90:12 - Buku Lopatulika12 Mutidziwitse kuwerenga masiku athu motero, kuti tikhale nao mtima wanzeru. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Mutidziwitse kuwerenga masiku athu motero, kuti tikhale nao mtima wanzeru. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Tsono tiphunzitseni kuŵerenga masiku athu, kuti tikhale ndi mtima wanzeru. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Tiphunzitseni kuwerenga masiku athu molondola, kuti tikhale ndi mtima wanzeru. Onani mutuwo |