Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 90:12 - Buku Lopatulika

12 Mutidziwitse kuwerenga masiku athu motero, kuti tikhale nao mtima wanzeru.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

12 Mutidziwitse kuwerenga masiku athu motero, kuti tikhale nao mtima wanzeru.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

12 Tsono tiphunzitseni kuŵerenga masiku athu, kuti tikhale ndi mtima wanzeru.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

12 Tiphunzitseni kuwerenga masiku athu molondola, kuti tikhale ndi mtima wanzeru.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 90:12
20 Mawu Ofanana  

Koma kwa munthu anati, Taonani, kuopa Ambuye ndiko nzeru; ndi kupatukana nacho choipa ndiko luntha.


Yehova, mundidziwitse chimaliziro changa, ndi mawerengedwe a masiku anga ndi angati; ndidziwe malekezero anga.


Onani, munaika masiku anga akhale monga kuyesa dzanja; ndipo zaka zanga zili ngati chabe pamaso panu, Indedi munthu aliyense angakhale wokhazikika, ali chabe konse.


Kodi kulandira nzeru sikupambana ndi golide, kulandira luntha ndi kusankhika koposa siliva?


Tchera makutu ako, numvere mau a anzeru, nulozetse mtima wako kukadziwa zanga.


Lozetsa mtima wako kumwambo, ndi makutu ako ku mau anzeru.


Gula ntheradi, osaigulitsa; nzeru, ndi mwambo, ndi luntha.


Tenga nzeru, tenga luntha; usaiwale, usapatuke pa mau a m'kamwa mwanga;


Nzeru ipambana, tatenga nzeru; m'kutenga kwako konseko utenge luntha.


Kunka kunyumba ya maliro kupambana kunka kunyumba ya madyerero; pakuti kujako ndi matsiriziro a anthu onse; ndipo omwe ali ndi moyo adzakumbukirapo.


Chilichonse dzanja lako lichipeza kuchichita, uchichite ndi mphamvu yako; pakuti mulibe ntchito ngakhale kulingirira ngakhale kudziwa, ngakhale nzeru, kumanda ulikupitako.


Tiyenera kugwira ntchito za Iye wondituma Ine, pokhala pali msana; ukudza usiku pamene palibe munthu angakhoze kugwira ntchito.


Akadakhala nazo nzeru, akadazindikira ichi, akadasamalira chitsirizo chao!


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa