Masalimo 90:11 - Buku Lopatulika11 Adziwa mphamvu ya mkwiyo wanu ndani, ndi ukali wanu monga ayenera kukuopani? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Adziwa mphamvu ya mkwiyo wanu ndani, ndi ukali wanu monga ayenera kukuopani? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Kodi ndani amadziŵa kukula kwa mkwiyo wanu ndi ukali wanu, kupambana anthu okuwopani? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Kodi ndani amadziwa mphamvu ya mkwiyo wanu? Pakuti ukali wanu ndi waukulu ngati ulemu umene uyenera Inu. Onani mutuwo |