Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Masalimo 89:9 - Buku Lopatulika

9 Inu ndinu wakuchita ufumu pa kudzikuza kwa nyanja; pakuuka mafunde ake muwachititsa bata.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

9 Inu ndinu wakuchita ufumu pa kudzikuza kwa nyanja; pakuuka mafunde ake muwachititsa bata.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

9 Mumalamulira nyanja yaukali. Mafunde ake akakwera, Inu mumaŵakhalitsa bata.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

9 Mumalamula nyanja ya mafunde awukali; pamene mafunde ake awundana Inu mumawakhalitsa bata.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 89:9
14 Mawu Ofanana  

Akunga Yehova Mulungu wathu ndani? Amene akhala pamwamba patali,


Yehova anakhala pa chigumula, inde Yehova akhala mfumu kunthawi yonka muyaya.


Amene atontholetsa kukuntha kwa nyanja, kukuntha kwa mafunde ake, ndi phokoso la mitundu ya anthu.


Ndipo chilungamo chidzakhala mpango wa m'chuuno mwake, ndi chikhulupiriko chidzakhala mpango wa pa zimpso zake.


amene muchitira chifundo anthu zikwi; nimubwezera mphulupulu ya atate m'chifukwa cha ana ao a pambuyo pao, dzina lake ndi Mulungu wamkulu, wamphamvu, Yehova wa makamu;


Adzudzula nyanja, naiphwetsa, naumitsa mitsinje yonse; Basani ndi Karimele afota, ndi duwa la ku Lebanoni linyala.


Ndipo pamene iwo analowa m'ngalawamo, mphepo inaleka.


Ndipo anauka, nadzudzula mphepo, nati kwa nyanja, kuti, Tonthola, khala bata. Ndipo mphepo inaleka, ndipo kunagwa bata lalikulu.


Ndipo iwo anachita mantha aakulu, nanenana wina ndi mnzake, Uyu ndani nanga, kuti ingakhale mphepo ndi nyanja zimvera Iye?


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa