Masalimo 89:8 - Buku Lopatulika8 Yehova, Mulungu wa makamu, wamphamvu ndani wonga Inu, Yehova? Ndipo chikhulupiriko chanu chikuzingani. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Yehova, Mulungu wa makamu, wamphamvu ndani wonga Inu, Yehova? Ndipo chikhulupiriko chanu chikuzingani. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Inu Chauta, Mulungu Wamphamvuzonse, kodi ndani ali wamphamvu ngati Inu Chauta, amene muli okhulupirika pa zonse? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Inu Yehova Mulungu Wamphamvuzonse, ndani wofanana nanu? Yehova ndinu wamphamvu ndipo kukhulupirika kwanu kwakuzungulirani. Onani mutuwo |