Masalimo 89:6 - Buku Lopatulika6 Pakuti kuli yani kuthambo timlinganize ndi Yehova? Afanana ndi Yehova ndani mwa ana a amphamvu? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Pakuti kuli yani kuthambo timlinganize ndi Yehova? Afanana ndi Yehova ndani mwa ana a amphamvu? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Kodi ndani mu mlengalenga angathe kulingana ndi Chauta? Ndani pakati pa akumwamba amafanafana naye? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Pakuti ndani mu mlengalenga angalingane ndi Yehova? Ndani wofanana ndi Yehova pakati pa zolengedwa zakumwamba? Onani mutuwo |