Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Masalimo 89:16 - Buku Lopatulika

16 Akondwera m'dzina lanu tsiku lonse; ndipo akwezeka m'chilungamo chanu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

16 Akondwera m'dzina lanu tsiku lonse; ndipo akwezeka m'chilungamo chanu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

16 Iwowo amakondwa masiku onse chifukwa cha Inu, ndipo amatamanda kulungama kwanu.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

16 Amakondwera mʼdzina lanu tsiku lonse lathunthu; amasangalala koposa mʼchilungamo chanu.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 89:16
20 Mawu Ofanana  

Mudzitamandire ndi dzina lake loyera: mitima yao ya iwo ofunsira Yehova ikondwere.


Liu la Yehova lithyola mitengo yamkungudza; inde Yehova athyola mikungudza ya ku Lebanoni.


Liu la Yehova ligawa malawi a moto.


Pakuti mtima wathu udzakondwera mwa Iye, chifukwa takhulupirira dzina lake loyera.


Chilungamo chanu sindinachibise m'kati mwamtima mwanga; chikhulupiriko chanu ndi chipulumutso chanu ndinachinena; chifundo chanu ndi choonadi chanu sindinachibisire msonkhano waukulu.


Mwa Mulungu tidzitamanda tsiku lonse, ndipo dzina lanu tidzaliyamika kosatha.


Munalenga kumpoto ndi kumwera; Tabori ndi Heremoni afuula mokondwera m'dzina lanu.


Inu a nyumba ya Yakobo, tiyeni, tiyende m'kuwala kwa Yehova.


ndiyandikizitsa chifupi chilungamo changa sichidzakhala patali, ndipo chipulumutso changa sichidzachedwa; ndipo ndidzaika chipulumutso m'Ziyoni, cha kwa Israele ulemerero wanga.


Masiku ake Yuda adzapulumutsidwa, ndipo Israele adzakhala mokhazikika, dzina lake adzatchedwa nalo, ndilo Yehova ndiye chilungamo chathu.


Ndipo uziwerengera masabata a zaka asanu ndi awiri, zaka zisanu ndi ziwiri kasanu ndi kawiri; kotero kuti zaka za masabata a zaka asanu ndi awiri, zifikire zaka makumi anai kudza zisanu ndi zinai.


Pamenepo uzitumizira lipenga lomveka m'mwezi wachisanu ndi chiwiri, tsiku lakhumi la mweziwo; tsiku la chitetezero mutumizire lipenga lifikire m'dziko lanu lonse.


ndipo mzimu wanga wakondwera mwa Mulungu Mpulumutsi wanga,


Pakuti m'menemo chaonetsedwa chilungamo cha Mulungu chakuchokera kuchikhulupiriro kuloza kuchikhulupiriro: monga kwalembedwa, Koma munthu wolungama adzakhala ndi moyo ndi chikhulupiriro.


Ameneyo sanadziwe uchimo anamyesera uchimo m'malo mwathu; kuti ife tikhale chilungamo cha Mulungu mwa Iye.


ndi kupezedwa mwa Iye, wosati wakukhala nacho chilungamo changa cha m'lamulo, koma chimene cha mwa chikhulupiriro cha Khristu, chilungamocho chochokera mwa Mulungu ndi chikhulupiriro;


Kondwerani mwa Ambuye nthawi zonse: ndibwerezanso kutero, kondwerani.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa