Masalimo 89:11 - Buku Lopatulika11 Kumwamba ndi kwanu, dziko lapansi lomwe ndi lanu; munakhazika dziko lokhalamo anthu ndi kudzala kwake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Kumwamba ndi kwanu, dziko lapansi lomwe ndi lanu; munakhazika dziko lokhalamo anthu ndi kudzala kwake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Zakumwamba ndi zanu, dziko lapansi nalonso ndi lanu. Mudapanga dziko lonse ndi zonse zam'menemo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Mayiko akumwamba ndi anu ndiponso dziko lapansi ndi lanu; munapanga dziko lonse ndi zonse zili mʼmenemo. Onani mutuwo |