Masalimo 89:10 - Buku Lopatulika10 Mudathyola Rahabu, monga munthu wophedwa; munabalalitsa adani anu ndi mkono wa mphamvu yanu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Mudathyola Rahabu, monga munthu wophedwa; munabalalitsa adani anu ndi mkono wa mphamvu yanu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Mudatswanya chilombo cha m'nyanja ndi kuchisandutsa mtembo. Mudabalalitsa adani anu ndi mkono wanu wamphamvu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Munaphwanya Rahabe monga munthu wophedwa; ndi dzanja lanu lamphamvu munabalalitsa adani anu. Onani mutuwo |