Masalimo 88:7 - Buku Lopatulika7 Mkwiyo wanu utsamira pa ine, ndipo munandizunza ine ndi mafunde anu onse. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Mkwiyo wanu utsamira pa ine, ndipo munandizunza ine ndi mafunde anu onse. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Mkwiyo wanu ukundipsinja, mukundimiza ndi mafunde anu onse. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Ukali wanu ukundipsinja kwambiri, mwandiopseza kwambiri ndi mafunde anu onse. Sela Onani mutuwo |