Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Masalimo 88:6 - Buku Lopatulika

6 Munandiika kunsi kwa dzenje, kuli mdima, kozama.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

6 Munandiika kunsi kwa dzenje, kuli mdima, kozama.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

6 Inu mwandiika pansi penipeni pa dzenje m'malo akuya a mdima wandiweyani.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

6 Mwandiyika pansi pa dzenje penipeni, mʼmalo akuya a mdima waukulu.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 88:6
13 Mawu Ofanana  

M'mozamamo ndinakufuulirani, Yehova.


Pakuti mdani alondola moyo wanga; apondereza pansi moyo wanga; andikhalitsa mumdima monga iwo adafa kale lomwe.


Ndipo anandikweza kunditulutsa m'dzenje la chitayiko, ndi m'thope la pachithaphwi; nandipondetsa pathanthwe, nakhazika mayendedwe anga.


Chigumula chisandifotsere, ndipo chakuya chisandimize; ndipo asanditsekere pakamwa pake pa dzenje.


Pakuti chifundo chanu cha pa ine nchachikulu; ndipo munalanditsa moyo wanga kunsi kwa manda.


Njira ya oipa ikunga mdima; sadziwa chimene chiwaphunthwitsa.


Wanditsogolera, nandiyendetsa mumdima, si m'kuunika ai.


Ndinaitana dzina lanu, Yehova, ndili m'dzenje lapansi;


Ndipo ndinati, Ndatayika ndichoke pamaso panu; koma ndidzapenyanso Kachisi wanu wopatulika.


Ndadza Ine kuunika kudziko lapansi, kuti yense wokhulupirira Ine asakhale mumdima.


Pakuti wayaka moto mu mkwiyo wanga, utentha kumanda kunsi ukutha dziko lapansi ndi zipatso zake, nuyatsa maziko a mapiri.


mafunde oopsa a nyanja, akuwinduka thovu la manyazi a iwo okha; nyenyezi zosokera, zimene mdima wakuda bii udazisungikira kosatha.


Angelonso amene sanasunge chikhalidwe chao choyamba, komatu anasiya pokhala paopao, adawasunga m'ndende zosatha pansi pa mdima, kufikira chiweruziro cha tsiku lalikulu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa