Masalimo 88:6 - Buku Lopatulika6 Munandiika kunsi kwa dzenje, kuli mdima, kozama. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Munandiika kunsi kwa dzenje, kuli mdima, kozama. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Inu mwandiika pansi penipeni pa dzenje m'malo akuya a mdima wandiweyani. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Mwandiyika pansi pa dzenje penipeni, mʼmalo akuya a mdima waukulu. Onani mutuwo |