Masalimo 88:5 - Buku Lopatulika5 Wotayika pakati pa akufa, ngati ophedwa akugona m'manda, amene simuwakumbukiranso; ndipo anawadula kusiyana ndi dzanja lanu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Wotayika pakati pa akufa, ngati ophedwa akugona m'manda, amene simuwakumbukiranso; ndipo anawadula kusiyana ndi dzanja lanu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Ndili ngati munthu womsiya yekha pakati pa anthu akufa, ngati munthu wophedwa amene wagona m'manda. Ndili ngati anthu amene Inu simuŵakumbukiranso, popeza kuti ndi ochotsedwa m'manja mwanu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Ndayikidwa pambali pamodzi ndi anthu akufa, monga ophedwa amene agona mʼmanda, amene Inu simuwakumbukiranso, amene achotsedwa pa chisamaliro chanu. Onani mutuwo |